112. Ndinalingitsa mtima wanga ucite malemba anu,Kosatha, kufikira cimatiziro.
113. Ndidana nao a mitima iwiri;Koma ndikonda cilamulo canu.
114. Inu ndinu pobisalapo panga, ndi cikopa canga;Ndiyembekezera mau anu.
115. Mundicokere ocita zoipa inu;Kuti ndisunge malamulo a Mulungu wanga.
116. Mundicirikize monga mwa mau anu, kuti ndikhale ndi moyo;Ndipo ndisacite manyazi pa ciyembekezo canga.