Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 116:5-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Yehova ngwa cifundo ndi wolungama;Ndi Mulungu wathu ngwa nsoni.

6. Yehova asunga opusa;Ndidafoka ine, koma anandipulumutsa,

7. Ubwere moyo wanga ku mpumulo wako;Pakuti Yehova anakucitira cokoma.

8. Pakuti munalanditsa moyo wanga kuimfa,Maso anga kumisozi, Mapazi anga, ndingagwe.

9. Ndidzayenda pamaso pa Yehova M'dziko la amoyo.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 116