Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 113:6-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Nadzicepetsa apenyeZam'mwamba ndi za pa dziko lapansi.

7. Amene autsa wosauka lrumcotsa kupfumbi,Nakweza waumphawi kumcotsa kudzala.

8. Kuti amkhalitse pamodzi ndi akulu,Pamodzi ndi akulu a anthu ace.

9. Asungitsa nyumba mkazi wosaonamwana,Akhale mai wokondwera ndi ana.Haleluya.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 113