6. Nadzicepetsa apenyeZam'mwamba ndi za pa dziko lapansi.
7. Amene autsa wosauka lrumcotsa kupfumbi,Nakweza waumphawi kumcotsa kudzala.
8. Kuti amkhalitse pamodzi ndi akulu,Pamodzi ndi akulu a anthu ace.
9. Asungitsa nyumba mkazi wosaonamwana,Akhale mai wokondwera ndi ana.Haleluya.