9. Moabu ndiye mkhate wanga;Pa Edomu ndidzaponya nsapato yanga;Ndidzapfuulira Filistiya,
10. Adzandifikitsa ndani m'mudzi wa m'linga?Adzanditsogolera ndani ku Edomu?
11. Si ndinu Mulungu, amene mwatitayaOsaturuka nao magulu athu?
12. Tithandizeni mumsauko;Pakuti cipulumutso ca munthu ndi cabe.