34. Sanaononga mitunduyo ya anthu,Imene Mulungu adawauza;
35. Koma anasokonekerana nao amitundu,Naphunzira nchito zao:
36. Ndipo anatumikira mafano ao,Amene anawakhalira msampha:
37. Ndipo anapereka ana ao amuna ndi akazi nsembe ya kwa ziwanda,
38. Nakhetsa mwazi wosacimwa, ndi wo mwazi wa ana ao amuna ndi akazi,Amene anawaperekera nsembe mafano a Kanani;M'mwemo analidetsa dziko ndi mwaziwo.