Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 106:34-38 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

34. Sanaononga mitunduyo ya anthu,Imene Mulungu adawauza;

35. Koma anasokonekerana nao amitundu,Naphunzira nchito zao:

36. Ndipo anatumikira mafano ao,Amene anawakhalira msampha:

37. Ndipo anapereka ana ao amuna ndi akazi nsembe ya kwa ziwanda,

38. Nakhetsa mwazi wosacimwa, ndi wo mwazi wa ana ao amuna ndi akazi,Amene anawaperekera nsembe mafano a Kanani;M'mwemo analidetsa dziko ndi mwaziwo.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 106