22. Zodabwiza m'dziko la Hamu,Zoopsa ku Nyanja Yofiira.
23. Potero Iye adati awaononge,Pakadapanda Mose wosankhika wace, kuima pamaso pace pagamukapo,Kubweza ukali wace ungawaononge,
24. Anapeputsanso dziko lofunika,Osabvomereza mau ace;
25. Koma anadandaula m'mahema mwao,Osamvera mau a Yehova.
26. Potero anawasamulira dzanja lace,Kuti awagwetse m'cipululu: