Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 106:22-26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

22. Zodabwiza m'dziko la Hamu,Zoopsa ku Nyanja Yofiira.

23. Potero Iye adati awaononge,Pakadapanda Mose wosankhika wace, kuima pamaso pace pagamukapo,Kubweza ukali wace ungawaononge,

24. Anapeputsanso dziko lofunika,Osabvomereza mau ace;

25. Koma anadandaula m'mahema mwao,Osamvera mau a Yehova.

26. Potero anawasamulira dzanja lace,Kuti awagwetse m'cipululu:

Werengani mutu wathunthu Masalmo 106