Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 106:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Haleluya.Yamikani Yehova; pakuti Iye ndiye wabwino:Pakuti cifundo cace ncosatha.

2. Adzafotokoza ndani nchito zamphamvu za Yehova,Adzamveketsa ndani cilemekezo cace conse?

3. Odala iwo amene asunga ciweruzo,Iye amene acita cilungamo nthawi zonse.

4. Mundikumbukile, Yehova, monga momwe mubvomerezana ndi anthu anu;Mundionetsa cipulumutso canu:

Werengani mutu wathunthu Masalmo 106