Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 105:35-40 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

35. Ndipo zinadya zitsamba zonse za m'dziko mwao,Zinadyanso zipatso za m'nthaka mwao.

36. Ndipo Iye anapha acisamba onse m'dziko mwaoCoyambira ca mphamvu yao yonse.

37. Ndipo anawaturutsa pamodzi ndi siliva ndi golidi:Ndi mwa mafuko ao munalibe mmodzi wokhumudwa.

38. Aigupto anakondwera pakucoka iwo;Popeza kuopsa kwao kudawagwera.

39. Anayala mtambo uwaphimbe;Ndi moto uunikire usiku,

40. Anafunsa ndipo Iye anadzetsa zinziri.Nawakhuritsa mkate wakumwamba.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 105