Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 102:9-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. Pakuti ndadya mapulusa ngati mkate,Ndi kusanganiza-comwera canga ndi misozi,

10. Cifukwa ca ukali wanu ndi kuzaza kwanu;Popeza munandinyamula ndipo munandigwetsa.

11. Masiku anga akunga mthunzi womka m'tali;Ndipo ine ndauma ngati udzu.

12. Koma Inu, Yehova, mukhalabe ku nthawi yonse;Ndi cikumbukilo canu ku mibadwo mibadwo.

13. Inu mudzauka, ndi kucitira nsoni Ziyoni;Popeza yafika nyengo yakumcitira cifundo, nyengo yoikika.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 102