Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 101:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndidzayimba za cifundo ndi ciweruzo;Ndidzayimba zakukulemekezani Inu, Yehova.

2. Ndidzacita mwanzeru m'njira yangwiro;Mudzandidzera liti?Ndidzayenda m'nyumba mwanu ndi mtima wangwiro.

3. Sindidzaika cinthu coipa pamaso panga;Cocita iwo akupatuka padera cindiipira;Sicidzandimamatira.

4. Mtima wopulukira udzandicokera;Sindidzadziwana naye woipa.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 101