Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Maliro 3:59-64 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

59. Yehova, mwaona coipa anandicitiraco, mundiweruzire;

60. Mwaona kubwezera kwao konse ndi zopangira zao zonse za pa ine.

61. Mwamva citonzo cao, Yehova, ndi zopangira zao zonse za pa ine,

62. Milomo ya akutsutsana nane ndi zolingalira zao za pa ine tsiku lonse.

63. Taonani kukhala ndi kunyamuka kwao; ndine nyimbo yao.

64. Mudzawabwezera cilango, Yehova, monga mwa macitidwe a manja ao;

Werengani mutu wathunthu Maliro 3