53. Anaononga moyo wanga m'dzenje, naponya mwala pamwambapaine;
54. Madzi anayenda pamwamba pa mutu panga, ndinati, dalikhidwa.
55. Ndinaitana dzina lanu, Yehova, ndiri m'dzenje lapansi;
56. Munamva mau anga; musabise khutu lanu popuma ndi popfuulaine.
57. Munayandikira tsiku la kukuitanani ine; munati, Usaope.
58. Ambuye munanenera moyo wanga mirandu yace; munaombola moyo wanga.
59. Yehova, mwaona coipa anandicitiraco, mundiweruzire;
60. Mwaona kubwezera kwao konse ndi zopangira zao zonse za pa ine.
61. Mwamva citonzo cao, Yehova, ndi zopangira zao zonse za pa ine,