Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Maliro 3:37-42 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

37. Ndani anganene, conena cace ndi kucitikadi, ngati Ambuye salamulira?

38. Kodi m'kamwa mwa Wam'mwambamwamba simuturuka zobvuta ndi zabwino?

39. Kodi munthu wamoyo adandauliranji pokhala m'zocimwa zace?

40. Tisanthule ntiyese njira zathu ntibwerenso kwa Yehova.

41. Titukulire mitima yathu ndi, manja athu omwe kwa Mulungu ali kumwamba.

42. Ife tilakwa ndi kupikisana nanu, ndipo Inu simunatikhululukira.

Werengani mutu wathunthu Maliro 3