Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Maliro 3:34-40 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

34. Kupondereza andende onse a m'dziko,

35. Kupambutsa ciweruzo ca munthu pamaso pa Wam'mwambamwamba,

36. Kukhotetsa mlandu wa munthu, zonsezi Ambuye sazikonda.

37. Ndani anganene, conena cace ndi kucitikadi, ngati Ambuye salamulira?

38. Kodi m'kamwa mwa Wam'mwambamwamba simuturuka zobvuta ndi zabwino?

39. Kodi munthu wamoyo adandauliranji pokhala m'zocimwa zace?

40. Tisanthule ntiyese njira zathu ntibwerenso kwa Yehova.

Werengani mutu wathunthu Maliro 3