Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Maliro 3:11-15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Wapambutsa njira zanga, nanding'amba; nandipululutsa.

12. Wathifula uta wace, nandiyesa polozetsa mubvi.

13. Walowetsa m'imso mwanga mibvi ya m'phodo mwace.

14. Ndasanduka wondiseka mtundu wanga wonse, ndi nyimbo yao tsiku lonse.

15. Wandidzaza ndi zowawa, wandikhutitsa civumulo.

Werengani mutu wathunthu Maliro 3