Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Malaki 3:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndidzayandikiza kwa inu kuti ndiweruze; ndipo ndidzakhala mboni yakufulumira kutsutsa obwebweta, ndi acigololo, ndi olumbira monama; ndi iwo akunyenga wolembedwa nchito pa kulipira kwace, akazi amasiye, ndi ana amasiye, ndi wakuipsa mlandu wa mlendo, osandiopa Ine, ati Yehova wa makamu.

Werengani mutu wathunthu Malaki 3

Onani Malaki 3:5 nkhani