Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Malaki 1:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mwana alemekeza atate wace, ndi mnyamata mbuye wace; ngati Ine tsono ndine atate, uli kuti ulemu wanga? ngati Ine ndine mbuye, kundiopa kuli kuti? ati Yehova wa makamu kwa inu ansembe akupeputsa dzina langa. Ndipo mukuti, Tapeputsa dzina lanu motani?

Werengani mutu wathunthu Malaki 1

Onani Malaki 1:6 nkhani