Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Malaki 1:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cinkana Edomu akuti, Taphwanyika, koma tidzabwera ndi kumanganso mabwinja; atero Yehova wa makamu, Adzamanga, koma Ine ndidzapasula; ndipo adzawacha, Dziko la coipa, ndiponso, Anthu amene Yehova akwiya nao cikwiyire.

Werengani mutu wathunthu Malaki 1

Onani Malaki 1:4 nkhani