Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 9:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ana a Aroni anasendera nao mwazi kwa iye; ndipo anabviika cala cace m'mwazimo naupaka pa nyanga za guwa la nsembe, nathira mwaziwo patsinde pa guwa la nsembe;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 9

Onani Levitiko 9:9 nkhani