Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 9:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo unaturuka mota pamaso ya Yehova, nunyeketsa nsembe yopsereza ndi mafuta pa guwa la nsembe; ndipo pakuciona anthu onse anapfuula, nagwa nkhope zao pansi.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 9

Onani Levitiko 9:24 nkhani