Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 5:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo akacimwa munthu, wakuti adamva mau akuwalumbiritsa, ndiye mboni, kapena wakuona, kapena wakudziwa, koma osaulula, azisenza mphulupulu yace;

2. kapena munthu akakhudza ciri conse codetsa kapena mtembo wa nyama yodetsa, kapena mtembo wa coweta codetsa, kapena mtembo wa cokwawa codetsa, kungakhale kudambisikira, ali wodetsedwa, ndi woparamula.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 5