Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 4:35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

nawacotse mafuta ace onse, monga umo amacotsera mafuta a nkhosa pa nsembe yoyamika; ndipo wansembeyo atenthe, awa pa guwa la nsembe, monga umo amacitira nsembe zamoto za Yehova; ndipo wansembeyo amcitire comtetezera pa kucimwa kwace adakucimwira, ndipo adzakhululukidwa.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 4

Onani Levitiko 4:35 nkhani