Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 3:16-17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Ndipo wansembe atenthe izi pa guwa la nsembe; ndizo cakudya ca nsembe yamoto icite pfungo lokoma; mafuta onse nga Yehova.

17. Likhale lemba losatha m'mibadwo yanu m'nyumba zanu zonse, musamadya kapena mafuta kapena mwazi.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 3