Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 22:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Munthu ali yense wa mbeu za Aroni wokhala ndi khate, kapena kukha, asadyeko zinthu zopatulika, kufikira atayera. Ndipo ali yense wokhudza cinthu codetsedwa ndi wakufa, kapena mwamuna wogona uipa;

Werengani mutu wathunthu Levitiko 22

Onani Levitiko 22:4 nkhani