Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 22:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Musamabwera nazo kwa Yehova yakhungu, kapenayodukamwendokapena yopunduka, kapena yapfundo, kapena yausemwe, kapena ya usemwe waukuru, musamazipereka kwa Yehova nsembe zamoto pa guwa la nsembe.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 22

Onani Levitiko 22:22 nkhani