Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 21:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Azikhala opatulikira Mulungu wao, osaipsa dzina la Mulungu wao; popeza amapereka nsembe zamoto za Yehova, mkate wa Mulungu wao; cifukwa cace akhale opatulika.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 21

Onani Levitiko 21:6 nkhani