Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 21:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wa mbeu ya Aroni wansembe asayandikize mmodzi wokhala naco cirema, kupereka nsembe zamoto za Yehova; ali naco cirema asayandikize kupereka cakudya ca Mulungu wace.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 21

Onani Levitiko 21:21 nkhani