Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 21:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nena ndi Aroni, kuti, Ali yense wa mbeu zako mwa mibadwo yao wakukhala naco cirema, asayandikize kupereka mkate wa Mulungu wace.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 21

Onani Levitiko 21:17 nkhani