Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 20:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ndanena nanu, Mudzalandira dziko lao inu, ndipo Ine ndilipereka kwa inu likhale lanu, ndilo dziko moyenda mkaka ndi uci ngati madzi; Ine ndine Yehova Mulungu wanu amene ndinakusiyanitsani ndi mitundu yina ya anthu.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 20

Onani Levitiko 20:24 nkhani