Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 19:3-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Ali yense aopemai wace, ndi atate wace; nimusunge masabata anga; Ine ndine Yehova Mulungu wanu.

4. Musamatembenukira mafano, kapena kudzipangira mulungu woyenga; Ine ndine Yehova Mulungu wanu.

5. Ndipo pamene muphera Yehova nsembe yoyamika, muiphere kuti mulandiridwe.

6. Tsiku lomwelo mwaipha, ndi m'mawa mwace muidye; ngati katsalirako kanthu tsiku lacitatu, muzikatentha ndi moto.

7. Akakadya konse tsiku tacitatu kali conyansa, kosabvomerezeka:

Werengani mutu wathunthu Levitiko 19