Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 19:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo wansembe acite comtetezera ndi nkhosa yamphongo ya nsembe yoparamula pamaso pa Yehova, cifukwa ca kucimwa adacimwaku; ndipo adzakhululukidwa cifukwa ca kucimwa kwace adacimwaku.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 19

Onani Levitiko 19:22 nkhani