Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 16:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ng'ombe ya nsembe yaucimo, ndi mbuzi ya nsembe yaucimo, zimene mwazi wao analowa nao kucita nao cotetezera m'malo opatulika, aturuke nazo kunja kwa cigono; natenthe ndi mota zikopa zao, ndi nyama zao, ndi cipwidza cao.

Werengani mutu wathunthu Levitiko 16

Onani Levitiko 16:27 nkhani