Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 13:12-14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Ndipo ngati khate libukabuka pakhungu, ndi khate lakuta khungu lonse la wanthendayo kuyambira mutu wace kufikira mapazi ace, monga momwe apenyera wansembe;

13. pamenepo wansembe aone, ndipo taonani, ngati khate lakuta thupi lace, amuche woyera wanthendayo; patuwa ponsepo; ndiye woyera.

14. Koma tsiku liri lonse ukaoneka pa iye mnofu wofiira, adzakhala wodetsedwa,

Werengani mutu wathunthu Levitiko 13