Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 10:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anapsa mtima pa Eleazara ndi Itamara, ana otsalawo a Aroni, nati, Mwalekeranji kudya nsembe yaucimo m'malo opatulika, pakuti ndiyo yopatulikitsa, ndipo iye anakupatsani iyo, kucotsera nayo mphulupulu ya khamulo, kuwacitira cowatetezera pamaso pa Yehova?

Werengani mutu wathunthu Levitiko 10

Onani Levitiko 10:17 nkhani