Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Hoseya 2:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndidzadzibzalira iye m'nthaka, ndipo ndidzacitira cifundo Wosacitidwa-cifundo; ndipo ndidzati kwa Si-anthu-anga, Muli anthu anga; ndipo iwo adzati, Ndinu Mulungu wathu.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 2

Onani Hoseya 2:23 nkhani