Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Hoseya 2:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsiku lomwelo ndidzawacitira pangano ndi nyama za kuthengo, ndi mbalame za mlengalenga, ndi zokwawa pansi; ndipo ndidzatyola uta, ndi lupanga, ndi nkhondo, zicoke m'dziko, ndi kuwagonetsa pansi mosatekeseka.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 2

Onani Hoseya 2:18 nkhani