Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Hagai 1:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. CAKA caciwiri ca mfumu Dariyo, mwezi wacisanu ndi cimodzi, mau a Yehova anadza mwa Hagai mneneri kwa Zerubabele mwana wa Sealitiyeli, ciwanga ca Yuda, ndi kwa Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, ndi kuti,

2. Atero Yehova wa makamu, akuti, Anthu awa anena, Nthawi siinafike, nthawi yakumanga nyumba ya Yehova.

3. Pamenepo mau a Yehova anadza mwa Hagai mneneri, ndi kuti,

Werengani mutu wathunthu Hagai 1