19. Tsoka iye wakunena kwa mtengo, Galamuka; ndi kwa mwala wosalankhula, Nyamuka Kodi ici ciphunzitsa? Taona cakutidwa ndi golidi ndi siliva, ndi m'kati mwace mulibe mpweya konse.
20. Koma Yehova ali m'Kacisi wace wopatulika; dziko lonse lapansi ale, cete pamaso pace.