Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 9:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kuopsya kwanu, ndi kucititsa mantha kwanu kudzakhala pa zinyama zonse za dziko lapansi, ndi pa zouluka zonse za m'mlengalenga; ndi pa zonse zokwawa pansi, ndi pa nsomba zonse za m'nyanja, zapatsidwa m'dzanja lanu.

Werengani mutu wathunthu Genesis 9

Onani Genesis 9:2 nkhani