Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 8:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anamva conunkhira cakukondweretsa; nati Yehova m'mtima mwace, Sindidzatembereranso konse nthaka cifukwa ca munthu; pakuti ndingaliro ya mtima wa munthu iri yoipa kuyambira pa unyamata wace; sindidzaphanso konse zinthu zonse zamoyo, monga momwe ndacitiramo.

Werengani mutu wathunthu Genesis 8

Onani Genesis 8:21 nkhani