Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 8:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Mulungu anakumbukira Nowa ndi zamoyo zonse, ndi nyama zonse zimene zinali pamodzi naye m'cingalawamo; ndipo Mulungu anapititsa mphepo pa dziko lapansi, naphwa madzi;

Werengani mutu wathunthu Genesis 8

Onani Genesis 8:1 nkhani