Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 7:23-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

23. Ndipo zinaonongedwa zamoyo zimene zonse zinali pa dziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa pa dzikolapansi: anatsala Nowayekha ndi amene anali pamodzi naye m'cingalawa.

24. Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Werengani mutu wathunthu Genesis 7