Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 6:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Mulungu anati kwa Nowa, Cimariziro cace ca anthu onse cafika pamaso panga; pakuti dziko lapansi ladzala ndi ciwawa cifukwa ca iwo; taonani, ndidzaononga iwo pamodzi ndi dziko lapansi.

Werengani mutu wathunthu Genesis 6

Onani Genesis 6:13 nkhani