Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 50:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yosefe ndipo anati kwa abale ace, Ndirinkufa ine, koma Mulungu adzaonekera kwa inu, adzakucotsani inu m'dziko muno kubwera kunka ku dziko limene analumbirira kwa Abrahamu ndi kwa Isake, ndi kwa Yakobo

Werengani mutu wathunthu Genesis 50

Onani Genesis 50:24 nkhani