Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 50:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo Yosefe anagwapa nkhope ya atate wace, namlirira iye nampsompsona iye.

2. Ndipo Yosefe anauza akapolo ace asing'anga kutiakonze atate wace: ndi mankhwala osungira thupi: ndipo asing'anga anakonza Israyeli.

3. Ndipo anatha masiku ace makumi anai a iye; cifukwa comweco amatsiriza masiku akukonza thupi; ndipo Aaigupto anamlira iye masiki makumi asanu ndi awiri.

4. Atapita masiku akumlira iye Yosefe anati kwa mbumba ya Farao kuti, Ngatitu ndapeza ufulu pamase panu, nenanitu m'makutu a Parae kuti,

Werengani mutu wathunthu Genesis 50