Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 49:31-33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

31. pamenepo anaika Abrahamu ndi Sara mkazi wace; pamenepo anaika Isake ndi Rebeka mkazi wace: pamenepo ndinaika Leya:

32. munda ndi phanga liri m'menemo, zinagulidwa kwa ana a Heti.

33. Pamene Yakobo anatha kulangiza ana ace amuna, anafunya mapazi ace pakama, natsirizika, nasonkhanizidwa kwa anthu a mtundu wace.

Werengani mutu wathunthu Genesis 49