Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 49:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Adamanga mwana wa kavalo wace pampesa,Ndi mwana wa buru wace pa mpesa wosankhika;Natsuka malaya ace m'vinyo,Ndi copfunda cace m'mwazi wa mphesa.

Werengani mutu wathunthu Genesis 49

Onani Genesis 49:11 nkhani