Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 48:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma anakana atate wace, nati, Ndidziwa mwananga, ndidziwa; Iyenso adzakhala mtundu wa anthu, iyenso adzakula; koma mphwace adzakhala wamkuru ndi iye, ndipo mbeu zace zidzakhala mitundu yambirimbiri.

Werengani mutu wathunthu Genesis 48

Onani Genesis 48:19 nkhani