Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 47:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yosefe anakhazika atate wace ndi abale ace, napatsa iwo pokhala m'dziko la Aigupto, m'dera lokometsetsa la m'dziko, m'dziko la Ramese, monga analamulira Farao.

Werengani mutu wathunthu Genesis 47

Onani Genesis 47:11 nkhani