Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 46:31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yosefe anati kwa abale ace, ndi kwa mbumba ya atate wace, Ndidzanka, ndikauze Farao, ndipo ndidzati kwa iye, Abale anga ndi mbumba ya atate wanga, amene anali m'dziko la Kanani, afika kwa ine;

Werengani mutu wathunthu Genesis 46

Onani Genesis 46:31 nkhani